Mpingo wa Time of Repenting and Deliverance Ministries (TIRDEM),wapereka mbewu ya chimanga kwa amayi amasiye ndi okalamba

M’busa wamkulu wa mpingowu, Mtumwi Albert Mpende wati mpingowu wachita izi pozindikira kuti mbewu za alimi ambiri zidapserera kamba ka ng’amba zomwe zadzetsa njala maka madera a m’boma la Chikwawa.

Pemenepa, iwo apempha amayiwa kuti asagulitse mbewuzi koma akabzale kuti akazakolola adzthe kupeza chakudya chokwanila pa banja pawo

Wolemba: Chifundo Bwalamba

Related posts

Magulu a alimi mzimbe a Kasinthula Can Growers Association m’boma la Chikwawa, pa 10 Epulo 2025 asankha Amade Alide kukhala wapampando wa alimiwa.

NZIKA ZACHITA ZOKAMBIRANA NDI ACHITETEZO

Kampani ya Illovo Sugar Malawi mogwirizana ndi bungwe la Catholic Relief Services (CRS) komanso boma la malawi yamanga nyumba zomwe ndizolimbana ndikusitha kwa nyengo.