Maerewa akhazikitsidwa lachitatu pa 21 may 2025 pamene wailesiyi yamaliza zokambilana zake ndi kampani yochititsa maere ya Supa win Malingana ndi yemwe…
Poyankhula Nardin Kamba bwanamkubwa wa boma la Chikwawa wapempha aphunzitsi kuti azilimbikira ntchito yawo poti boma likuyetsetsa kuwaganizira pofuna kukwaniritsa masomphenya a…
wanena izi ndi modzi mwa akuluakulu ku bungweli,mayi Hope Gee Williams pa mwambo olimbikitsa ufulu wa anthu,womwe unachitikila pa sukulu ya sekondale…
Akuluakulu a Kampani ya UNITRANS achenjeza anthu kuti azikhala a tcheru pamene galimoto zawo zikuluzikulu zonyamula mzimbe zikudutsa m’misewu m’madera awo pofuna…
Yemwe akuyimira chipani cha UTM ngati Phungu wa Nyumba ya Malamulo pakati Boma la Chikwawa pa chisankho cha pa 16 September pano,…
Alimi a mzimbe okwana 762 ndi omwe atenga nawo mbali pa chisankhochi chomwe chinachitikira ku maofesi a zaulimi a Kasinthula pa msonkhano…
M’busa wamkulu wa mpingowu, Mtumwi Albert Mpende wati mpingowu wachita izi pozindikira kuti mbewu za alimi ambiri zidapserera kamba ka ng’amba zomwe…
Gulu la Dyeratu Nzika Lachisanu lidayitanitsa magulu a chitetezo chakumudzi a Community Policing Forum (CPF) pa zokambirana pa sukulu ya pulayimare ya…
Ogwira ntchito komanso odwala pa chipatala cha Makhuwira adandaula kuti amavutika ndi madzi omwe amasefukira mu Mtsinje wa Thelhiwani ponena kuti amasokoneza…