Boma la Malawi kudzera ku khonsolo ya boma la Chikwawa lakweza pantchito aphunzitsi a m’sukulu za pulayimale pafupifupi 900 a m’bomali.

Poyankhula Nardin Kamba bwanamkubwa wa boma la Chikwawa wapempha aphunzitsi kuti azilimbikira ntchito yawo poti boma likuyetsetsa kuwaganizira pofuna kukwaniritsa masomphenya a dziko Malawi 2063.

Nawo a Gertrude Jumbe mkulu wa zamaphunziro m’bomali wagwirizana ndi pempho la bwanamkubwayu.

Naye Madalitso Nansolola ndi m’modzi mwa aphunzitsi a amayi yemwe wakwezedwa .

Iye wathokoza boma chifukwa ichi ati ndi chilimbik

Related posts

Wailesi ya Nyungwe yakhazikitsa maere omwe pakutha pa tsiku anthu oposera makumi atatu azikhala akuchita mphumi yopambana ndalama yosachepera 10,000 kwacha

Bungwe la center for human rights, Education,Advice and Assistance (CHREAA) lalangiza ophinzila achitsikana kuti azinena za nkhanza zogonana zomwe amakumanazo kwa adindo.

CHIPATALA CHA MAKHUWIRA CHILI PA CHIOPSEZO CHA MADZI OSEFUKIRA