Home Uncategorized AMUMANGA ATATAYIRA KHANDA M’CHIMBUDZI

AMUMANGA ATATAYIRA KHANDA M’CHIMBUDZI

by Robert Malenga
0 comments

#Nyungwe_FM_Nkhani

Kwa Ngabu m’boma la Chikwawa, apolisi ati amanga mayi ena a zaka 27 kamba kotayira mwana wobereka wokha m’chimbudzi chokumba kamba koti mwamuna wake adakana pathupi pa mwanayo.

Mneneri wa apolisi m’bomali, Sergeant Dickson Matemba wati maiyu adapalamula mlanduwu pa 23 March 2025 m’mudzi mwa Thobwa kwa Mfumu yaikulu Ngabu m’bomali.

Padakali pano apolisi m’bomali omwe adzudzula mchitidwewu ati atengera maiyu ku bwalo la milandu ndi kukayankha pa mlandu womwe akumuganizira kuti wapalamula.

Wolemba: Francis Mwale

#Liwu_la_Mchigwa

You may also like

Leave a Comment

Nyungwe FM 107.6MHz is located near Thabwa Road Block in Chikwawa district.
Voice of the valley.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00