#Nyungwe_FM_Nkhani Ntchito yomanga malo osambira pa chipatala chaching’ono cha Chavala m’dera la Mfumu yaikulu Kasisi m’boma la Chikwawa yayamba Lolemba pa 17 …
Category:
Uncategorized
-
-
Uncategorized
Mlangizi wa Zamaphunziro ku zone ya Boma m’boma la Chikwawa a Tobias Tembo ayamikira zomwe bungwe la Dyeratu Nzika lachita popereka mayunifolomu kwa ophunzira pa sukulu ya pulayimare ya Dyeratu m’bomali.
Nyungwe_FM_Nkhani Poyankhula ku m’mawa wa Lolemba pa 17 March 2025 pa mwambo wopereka zovalazi, a Tembo apempha ophunzirawa kuti azigwiritse ntchito pa …
-
#Nyungwe_FM_Nkhani Galimoto yonyamula katundu ya mtundu wa track panopa, yatseka msewu pa chipata cha malo ochitira chipikiseni cha apolisi pa Kamuzu Bridge …
-
Gulu la Dyeratu Nzika, Lachisanu pa 21 March 2025 lalandira maphunziro olimbikitsa nzika kutengapo mbali ndi kutsatira ndondomeko za zitukuko pa Khonsolo. …
-
Mphunzitsi wamkulu pa sukulu ya pulayimare ya Dyeratu m’boma la Chikwawa, a Dackford Jeremia ati sukuluyi ili pa vuto lopeza madzi aukhondo …
Older Posts