Home Uncategorized Bungwe la center for human rights, Education,Advice and Assistance (CHREAA) lalangiza ophinzila achitsikana kuti azinena za nkhanza zogonana zomwe amakumanazo kwa adindo.

Bungwe la center for human rights, Education,Advice and Assistance (CHREAA) lalangiza ophinzila achitsikana kuti azinena za nkhanza zogonana zomwe amakumanazo kwa adindo.

by Robert Malenga
0 comments

wanena izi ndi modzi mwa akuluakulu ku bungweli,mayi Hope Gee Williams pa mwambo olimbikitsa ufulu wa anthu,womwe unachitikila pa sukulu ya sekondale ya St Michaels boma la chikwawa.

Mayi Williams ati bungweli lachita izi pozindikila kuti atsikana ambili amabisa za nkhanza zomwe amakumana nazo tsiku ndi tsiku.ndipo mayi Williams ati nkumanowu unali wofunika kwambili kamba kuti wathandizila kuzindikilitsa atsikanawa zakuyipa kwa ma ukwati awana achichepele.

Mayi Williams alangiza ophunzilawa kuti akhazikitse ma gulu oti azithandizana komanso kulimbikitsana pa nkhani ya zamaphunzilo

wolemba:Robert Benson Malenga

You may also like

Leave a Comment

Nyungwe FM 107.6MHz is located near Thabwa Road Block in Chikwawa district.
Voice of the valley.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00